Numeri 12:3-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Koma munthuyu Mose ndiye wofatsa woposa anthu onse a pa dziko lapansi.

4. Ndipo Yehova anati kwa Mose, ndi Aroni, ndi Miriamu modzidzimutsa, Turukani inu atatu kudza ku cihema cokomanako. Pamenepo anaturuka atatuwo.

5. Ndipo Yehova anatsika mumtambo njo, naima pa khomo la cihema, naitana Aroni ndi Miriamu; naturuka onse awiri.

Numeri 12